1 Akorinto 1:4 - Buku Lopatulika4 Ndiyamika Mulungu wanga nthawi yonse kaamba ka inu, chifukwa cha chisomo cha Mulungu chinapatsidwa kwa inu mwa Khristu Yesu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndiyamika Mulungu wanga nthawi yonse kaamba ka inu, chifukwa cha chisomo cha Mulungu chinapatsidwa kwa inu mwa Khristu Yesu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Nthaŵi zonse ndimayamika Mulungu wanga chifukwa cha inu, popeza kuti adakukomerani mtima mwa Khristu Yesu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Nthawi zonse ndimayamika Mulungu chifukwa cha inu chifukwa cha chisomo chake chopatsidwa kwa inu mwa Khristu Yesu. Onani mutuwo |