1 Akorinto 1:5 - Buku Lopatulika5 kuti m'zonse munalemezedwa mwa Iye, m'mau onse, ndi chidziwitso chonse; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 kuti m'zonse munalemezedwa mwa Iye, m'mau onse, ndi chidziwitso chonse; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Zoonadi mwa Khristu mwakhala anthu olemera pa zonse, makamaka pa kulankhula ndi pa kudziŵa zinthu, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Pakuti mwa Iye mwalemekezedwa mʼnjira iliyonse, mʼkuyankhula kwanu konse ndi mʼkudziwa kwanu konse, Onani mutuwo |