Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Afilipi 1:2 - Buku Lopatulika

2 Chisomo kwa inu ndi mtendere za kwa Mulungu Atate wathu ndi Ambuye Yesu Khristu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Chisomo kwa inu ndi mtendere za kwa Mulungu Atate wathu ndi Ambuye Yesu Khristu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Mulungu Atate athu ndi Ambuye Yesu Khristu akukomereni mtima ndi kukupatsani mtendere.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Chisomo ndi mtendere zochokera kwa Mulungu Atate athu ndi Ambuye Yesu Khristu zikhale kwa inu.

Onani mutuwo Koperani




Afilipi 1:2
4 Mawu Ofanana  

kwa onse a ku Roma, okondedwa a Mulungu, oitanidwa kuti akhale oyera mtima: Chisomo chikhale ndinu ndi mtendere wa kwa Mulungu Atate wathu, ndi Ambuye Yesu Khristu.


Chisomo kwa inu ndi mtendere zochokera kwa Mulungu Atate wathu, ndi Ambuye Yesu Khristu.


Ndiyamika Mulungu wanga pokumbukira inu ponse;


monga mwa kudziwiratu kwa Mulungu Atate, m'chiyeretso cha Mzimu, chochitira chimvero, ndi kuwaza kwa mwazi wa Yesu Khristu: Chisomo, ndi mtendere zichulukire inu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa