Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 5:14 - Buku Lopatulika

Maina a iwo anambadwira mu Yerusalemu ndi awa: Samuwa, ndi Sobabu, ndi Natani, ndi Solomoni,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Maina a iwo anambadwira m'Yerusalemu ndi awa: Samuwa, ndi Sobabu, ndi Natani, ndi Solomoni,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Naŵa maina a ana a Davide amene adabadwira ku Yerusalemu: Samuwa, Sobabu, Natani, Solomoni,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mayina a ana amene anabereka ku Yerusalemu ndi awa: Samua, Sobabu, Natani, Solomoni,

Onani mutuwo



2 Samueli 5:14
9 Mawu Ofanana  

ndi Ibara ndi Elisuwa, ndi Nefegi ndi Yafiya;


ndi Azariya mwana wa Natani anayang'anira akapitao, ndipo Zabudi mwana wa Natani anali wansembe ndi nduna yopangira mfumu,


Maina a ana anali nao mu Yerusalemu ndi awa: Samuwa, ndi Sobabu Natani, ndi Solomoni,


Ndipo dziko lidzalira, banja lililonse pa lokha; banja la nyumba ya Davide pa lokha, ndi akazi ao pa okha; banja la nyumba ya Natani pa lokha, ndi akazi ao pa okha;


ndi Yese anabala Davide mfumuyo. Ndipo Davide anabala Solomoni mwa mkazi wa Uriya;


chimene munakonza pamaso pa anthu onse,