Zekariya 12:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo dziko lidzalira, banja lililonse pa lokha; banja la nyumba ya Davide pa lokha, ndi akazi ao pa okha; banja la nyumba ya Natani pa lokha, ndi akazi ao pa okha; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo dziko lidzalira, banja lililonse pa lokha; banja la nyumba ya Davide pa lokha, ndi akazi ao pa okha; banja la nyumba ya Natani pa lokha, ndi akazi ao pa okha; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Dziko lidzalira, banja lililonse palokha. Banja la Davide lidzalira palokha, akazi akenso adzalira paokha. Banja la Natani lidzalira palokha, akazi akenso adzalira paokha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Dziko lidzalira kwambiri, fuko lililonse pa lokha, akazi awo pa okhanso: fuko la Davide pamodzi ndi akazi awo, fuko la Natani pamodzi ndi akazi awo, Onani mutuwo |