1 Mafumu 4:5 - Buku Lopatulika5 ndi Azariya mwana wa Natani anayang'anira akapitao, ndipo Zabudi mwana wa Natani anali wansembe ndi nduna yopangira mfumu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 ndi Azariya mwana wa Natani anayang'anira akapitao, ndipo Zabudi mwana wa Natani anali wansembe ndi nduna yopangira mfumu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Azariya mwana wa Natani ankayang'anira nduna zam'zigawo. Zabudi mwana wa Natani anali wansembe ndi mlangizi wapadera wa mfumu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Azariya mwana wa Natani, anali woyangʼanira nduna za mʼzigawo; Zabudi mwana wa Natani, anali wansembe ndi bwenzi la mfumu; Onani mutuwo |