Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 3:11 - Buku Lopatulika

Ndipo iye sanakhoze kuyankha Abinere mau amodzi chifukwa cha kumuopa iye.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo iye sanakhoze kuyankha Abinere mau amodzi chifukwa cha kumuopa iye.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamenepo Isiboseti adangoti kukamwa yasa, osatha kumuyankha Abinere mau ndi amodzi omwe, chifukwa ankamuwopa kwambiri.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Isiboseti sanayerekezenso kunena mawu ena kwa Abineri, chifukwa ankamuopa.

Onani mutuwo



2 Samueli 3:11
3 Mawu Ofanana  

kuchotsa ufumu kunyumba ya Saulo ndi kukhazika mpando wachifumu wa Davide pa Israele ndi pa Yuda, kuyambira ku Dani kufikira ku Beereseba.


Ndipo Abinere anatuma mithenga imnenere kwa Davide, nati, Dziko nla yani? Natinso, Mupangane nane pangano lanu, ndipo onani, ndidzagwirizana nanu ndi kukopa Aisraele onse atsate inu.


Mwagwedeza dziko, mwaling'amba. Konzani ming'alu yake; pakuti ligwedezeka.