Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Samueli 3:11 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Isiboseti sanayerekezenso kunena mawu ena kwa Abineri, chifukwa ankamuopa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

11 Ndipo iye sanakhoze kuyankha Abinere mau amodzi chifukwa cha kumuopa iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Ndipo iye sanakhoze kuyankha Abinere mau amodzi chifukwa cha kumuopa iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Pamenepo Isiboseti adangoti kukamwa yasa, osatha kumuyankha Abinere mau ndi amodzi omwe, chifukwa ankamuwopa kwambiri.

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 3:11
3 Mawu Ofanana  

Ndidzachotsa ufumu ku nyumba ya Sauli ndi kukhazikitsa ufumu wa Davide pa Aisraeli onse ndi Yuda kuchokera ku Dani mpaka ku Beeriseba.”


Kenaka Abineri anatuma amithenga kwa Davide kukanena kuti, “Kodi dzikoli ndi la yani? Uchite mgwirizano ndi ine ndipo ndidzakuthandiza kuti Aisraeli onse azikutsatira.”


Inu mwagwedeza dziko ndipo mwalingʼamba, konzani mingʼalu yake pakuti ikugwedezeka kwambiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa