Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 22:30 - Buku Lopatulika

Pakuti ndi Inu ndithamangira gulu; ndi Mulungu wanga ndilumphira linga.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti ndi Inu ndithamangira gulu; ndi Mulungu wanga ndilumphira linga.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndi chithandizo chanu ndingathe kugonjetsa gulu la ankhondo. Ndi chithangato chanu, Inu Mulungu, ndingathe kupambana.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndi thandizo lanu nditha kulimbana ndi gulu la ankhondo, ndi Mulungu wanga nditha kuchita zosatheka ndi munthu.

Onani mutuwo



2 Samueli 22:30
6 Mawu Ofanana  

Kunena za Mulungu, njira yake ili yangwiro; mau a Yehova anayesedwa; Iye ndiye chikopa kwa onse akukhulupirira Iye.


Ndipo mfumu ndi anthu ake anamuka ku Yerusalemu kuyambana nao Ayebusi, nzika za dziko; ndiwo ananena kwa Davide ndi kuti, Sudzalowa muno, koma akhungu ndi opunduka adzakupirikitsa; ndiko kunena kuti, Davide sangathe kulowa muno.


Pakuti mwa Inu ndipyola khamu la anthu; ndipo mwa Mulungu wanga ndilumphira linga.


Koma m'zonsezi, ife tilakatu, mwa Iye amene anatikonda.


Ndikhoza zonse mwa Iye wondipatsa mphamvuyo.