Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 22:19 - Buku Lopatulika

Anandifikira ine tsiku la tsoka langa; koma Yehova anali mchirikizo wanga.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Anandifikira ine tsiku la tsoka langa; koma Yehova anali mchirikizo wanga.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adaniwo adandithira nkhondo pamene ndinali m'mavuto, koma Chauta adandichirikiza.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Adaniwo analimbana nane pamene ndinali pa mavuto, koma Yehova anali thandizo langa.

Onani mutuwo



2 Samueli 22:19
12 Mawu Ofanana  

Iye anandipulumutsa kwa mdani wanga wamphamvu, kwa iwo akudana ndi ine; pakuti anandiposa mphamvu.


Inde, ndingakhale ndiyenda m'chigwa cha mthunzi wa imfa, sindidzaopa choipa; pakuti Inu muli ndi ine; chibonga chanu ndi ndodo yanu, izi zindisangalatsa ine.


Akufa anu adzakhala ndi moyo; mitembo yao idzauka. Ukani muimbe, inu amene mukhala m'fumbi; chifukwa mame ako akunga mame a pamasamba, ndipo dziko lapansi lidzatulutsa mizimu.


usaope, pakuti Ine ndili pamodzi ndi iwe; usaopsedwe, pakuti Ine ndine Mulungu wako; ndidzakulimbitsa; inde, ndidzakuthangata; inde, ndidzakuchirikiza ndi dzanja langa lamanja la chilungamo.


Ndani ali mwa inu amene amaopa Yehova, amene amamvera mau a mtumiki wake? Iye amene ayenda mumdima, ndipo alibe kuunika, akhulupirire dzina la Yehova, ndi kutsamira Mulungu wake.