Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 22:13 - Buku Lopatulika

Cheza cha pamaso pake makala a moto anayaka.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Cheza cha pamaso pake makala a moto anayaka.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

M'kuŵala kumene kunali pamaso pake munkafumira makala amoto alaŵilaŵi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mʼkuwala kumene kunali pamaso pake munkachokera makala amoto alawilawi.

Onani mutuwo



2 Samueli 22:13
3 Mawu Ofanana  

Yehova anagunda kumwamba; ndipo Wam'mwambamwamba ananena mau ake.


M'mphuno mwake munatuluka utsi, ndi moto wotuluka m'kamwa mwake unaononga; makala anayaka nao.


Ndipo maonekedwe a ulemerero wa Yehova anali ngati moto wonyeketsa pamwamba paphiri, pamaso pa ana a Israele.