Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 15:17 - Buku Lopatulika

Ndipo mfumu inatuluka, ndi anthu onse anamtsata; naima kunyumba ya pa yokha.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo mfumu inatuluka, ndi anthu onse anamtsata; naima kunyumba ya pa yokha.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene mfumu idatuluka, anthu onse adaitsata. Onsewo adakaima pa nyumba yomalizira.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kotero mfumu inanyamuka pamodzi ndi anthu onse oyitsatira, ndipo anayima pamalo pena chapatalipo.

Onani mutuwo



2 Samueli 15:17
5 Mawu Ofanana  

Mfumu nituluka, ndi banja lake lonse linamtsata. Ndipo mfumu inasiya akazi khumi ndiwo akazi aang'ono, kusunga nyumbayo.


Ndipo anyamata ake onse anapita naye limodzi; ndi Akereti ndi Apeleti, ndi Agiti onse, anthu mazana asanu ndi limodzi omtsata kuchokera ku Gati, anapita pamaso pa mfumu.


Munapititsa anthu oberekeka pamwamba pamitu pathu; tinapyola moto ndi madzi; koma munatifikitsa potitsitsimutsa.


Ndaona akapolo atakwera pa akavalo, ndi mafumu, alikuyenda pansi ngati akapolo.