Masalimo 66:12 - Buku Lopatulika12 Munapititsa anthu oberekeka pamwamba pamitu pathu; tinapyola moto ndi madzi; koma munatifikitsa potitsitsimutsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Munapititsa anthu oberekeka pamwamba pamitu pathu; tinapyola moto ndi madzi; koma munatifikitsa potitsitsimutsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Inu mudalola kuti adani atikwere pa mutu, tidaloŵa m'moto ndiponso m'madzi, komabe Inu mwatifikitsa ku malo opulumukirako. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Inu munalola kuti anthu akwere pa mitu yathu; ife tinadutsa mʼmoto ndi mʼmadzi, koma Inu munatibweretsa ku malo a zinthu zochuluka. Onani mutuwo |