Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 66:11 - Buku Lopatulika

11 Munapita nafe kuukonde; munatisenza chothodwetsa pamsana pathu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Munapita nafe kuukonde; munatisenza chothodwetsa pamsana pathu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Inu mudatiloŵetsa mu ukonde wa adani, mudatisenzetsa katundu wolemera pamsana pathu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Inu mwatilowetsa mʼndende ndi kutisenzetsa zolemera pa misana yathu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 66:11
7 Mawu Ofanana  

Dziwani tsopano kuti Mulungu wandikhotetsera mlandu wanga, nandizinga ndi ukonde wake.


Anatumiza moto wochokera kumwamba kulowa m'mafupa anga, unawagonjetsa; watchera mapazi anga ukonde, wandibwezera m'mbuyo; wandipululutsa ndi kundilefula tsiku lonse.


Ndidzamphimba ndi ukonde wanga, nadzakodwa iye mu msampha wanga; ndipo ndidzafika naye ku Babiloni, ku dziko la Ababiloni; sadzaliona, chinkana adzafako.


Pamene amuka ndidzawayalira ukonde wanga, ndidzawagwetsa ngati mbalame za m'mlengalenga, ndidzawalanga monga udamva msonkhano wao.


Ndipo musatitengere kokatiyesa, koma mutipulumutse kwa woipayo.


Dalitsani, Yehova, mphamvu yake, nimulandire ntchito ya manja ake; akantheni m'chuuno iwo akumuukira, ndi iwo akumuda, kuti asaukenso.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa