Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mlaliki 10:7 - Buku Lopatulika

7 Ndaona akapolo atakwera pa akavalo, ndi mafumu, alikuyenda pansi ngati akapolo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Ndaona akapolo atakwera pa akavalo, ndi mafumu, alikuyenda pansi ngati akopolo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Ndaona akapolo akuyenda pa akavalo, m'menemo akalonga akuyenda pansi ngati akapolo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Ndaona akapolo atakwera pa akavalo, pamene akalonga akuyenda pansi ngati akapolo.

Onani mutuwo Koperani




Mlaliki 10:7
4 Mawu Ofanana  

Ndipo mfumu inatuluka, ndi anthu onse anamtsata; naima kunyumba ya pa yokha.


amtengere chovala chachifumu amachivala mfumu, ndi kavalo amakwerapo mfumu, naike korona wachifumu pamutu pake,


Wopusa sayenera kukhala ndi zinthu zolongosoka; nanga kapolo ayenera kulamulira akalonga kodi?


chifukwa cha kapolo pamene ali mfumu; ndi chitsiru chitakhuta zakudya;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa