Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mlaliki 10:6 - Buku Lopatulika

6 utsiru ukhazikika pamwamba penipeni, ndipo olemera angokhala mwamanyazi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 utsiru ukhazikika pamwamba penipeni, ndipo olemera angokhala mwamanyazi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Opusa amaŵapatsa ntchito zapamwamba, olemera nkumaŵapatsa ntchito zotsika.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Zitsiru amazipatsa ntchito zambiri zapamwamba, pamene anthu olemera amawapatsa ntchito zotsika.

Onani mutuwo Koperani




Mlaliki 10:6
11 Mawu Ofanana  

Zitatha izi, mfumu Ahasuwero anamkuza Hamani mwana wa Hamedata, wa ku Agagi, namkweza, naika mpando wake upose akalonga onse okhala naye.


Ndipo Hamani, pakuona kuti Mordekai sanamweramire kapena kumgwadira, mtima wake unadzala mkwiyo.


Oipa amayenda mozungulirazungulira, potamanda iwo chonyansa mwa ana a anthu.


Wopusa sayenera kukhala ndi zinthu zolongosoka; nanga kapolo ayenera kulamulira akalonga kodi?


Posekera olungama pali ulemerero wambiri; koma pouka oipa anthu amabisala.


Pouka oipa anthu amabisala; koma pakufa amenewo olungama achuluka.


Pochuluka olungama anthu akondwa; koma polamulira woipa anthu ausa moyo.


Pali choipa ndachiona pansi pano, ngati kulakwa koyambira ndi mkulu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa