Mlaliki 10:5 - Buku Lopatulika5 Pali choipa ndachiona pansi pano, ngati kulakwa koyambira ndi mkulu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Pali choipa ndachiona pansi pano, ngati kulakwa koyambira ndi mkulu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Pansi pano pali choipa china chimene ndachiwona, choipa chake ndi cholakwa chimene amachichita wolamula. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Pali choyipa chimene ndinachiona pansi pano, kulakwitsa kumene kumachokera kwa wolamulira: Onani mutuwo |