Mlaliki 10:8 - Buku Lopatulika8 Wokumba mbuna adzagwamo; ndipo woboola mpanda njoka idzamluma. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Wokumba mbuna adzagwamo; ndipo woboola mpanda njoka idzamluma. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Amene amakumba dzenje adzagwamo yekha. Amene amaboola khoma njoka idzamuluma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Amene amakumba dzenje adzagwamo yekha; amene amabowola khoma adzalumidwa ndi njoka. Onani mutuwo |