Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mlaliki 10:9 - Buku Lopatulika

9 Wosendeza miyala adzaphwetekedwa nayo; wowaza nkhuni nadzitema.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Wosendeza miyala adzaphwetekedwa nayo; wowaza nkhuni nadzitema.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Amene amakumba miyala, itha kumpweteka miyalayo. Amene amaŵaza nkhuni, atha kudzipweteka nazo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Amene amaphwanya miyala adzapwetekedwa ndi miyalayo; amene amawaza nkhuni adzapwetekedwa nazo.

Onani mutuwo Koperani




Mlaliki 10:9
2 Mawu Ofanana  

Chitsulo chikakhala chosathwa, ndipo ukaleka kunola, uzipambana kulimbikira; koma nzeru ipindulira pochenjeza.


Wokumba mbuna adzagwamo; ndipo woboola mpanda njoka idzamluma.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa