Mlaliki 10:10 - Buku Lopatulika10 Chitsulo chikakhala chosathwa, ndipo ukaleka kunola, uzipambana kulimbikira; koma nzeru ipindulira pochenjeza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Chitsulo chikakhala chosathwa, ndipo ukaleka kunola, uzipambana kulimbikira; koma nzeru ipindulira pochenjeza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Nkhwangwa ikakhala yobuntha, nkupandanso kuinola, imalira mphamvu zambiri potema. Koma nzeru zimathandiza munthu kuti athedi kudula kanthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ngati nkhwangwa ili yobuntha yosanoledwa, pamafunika mphamvu zambiri potema, koma luso limabweretsa chipambano. Onani mutuwo |