Mlaliki 10:11 - Buku Lopatulika11 Njoka ikaluma isanalodzedwe, watsenga saona mphotho. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Njoka ikaluma isanalodzedwe, watsenga saona mphotho. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Nkopanda phindu kudziŵa kuseŵeretsa njoka ngati njokayo yakuluma kale. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Nʼkopanda phindu kudziwa kuseweretsa njoka ngati njokayo yakuluma kale. Onani mutuwo |