Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mlaliki 10:11 - Buku Lopatulika

11 Njoka ikaluma isanalodzedwe, watsenga saona mphotho.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Njoka ikaluma isanalodzedwe, watsenga saona mphotho.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Nkopanda phindu kudziŵa kuseŵeretsa njoka ngati njokayo yakuluma kale.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Nʼkopanda phindu kudziwa kuseweretsa njoka ngati njokayo yakuluma kale.

Onani mutuwo Koperani




Mlaliki 10:11
9 Mawu Ofanana  

Lilime lako likupanga zoipa; likunga lumo lakuthwa, lakuchita monyenga.


Thyolani mano ao m'kamwa mwao, Mulungu, zulani zitsakano za misona ya mkango, Yehova.


Amene anola lilime lao ngati lupanga, napiringidza mivi yao, ndiyo mau akuwawitsa;


Lilime lili ndi mphamvu pa imfa ndi moyo; wolikonda adzadya zipatso zake.


Chitsulo chikakhala chosathwa, ndipo ukaleka kunola, uzipambana kulimbikira; koma nzeru ipindulira pochenjeza.


Pakuti, taonani, ndidzatumiza pa inu njoka, mphiri, zosalola kuitanidwa; ndipo zidzakulumani inu, ati Yehova.


Ndipo lilime ndilo moto; ngati dziko la chosalungama mwa ziwalo zathu laikika lilime, ndili lodetsa thupi lonse, niliyatsa mayendedwe a chibadwidwe, ndipo liyatsidwa ndi Gehena.


koma lilime palibe munthu akhoza kulizoloweretsa; lili choipa chotakataka, lodzala ndi ululu wakupha.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa