Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 8:2 - Buku Lopatulika

Dzina la mwana wake woyamba ndiye Yowele, ndi dzina la wachiwiri ndiye Abiya; ndiwo oweruza a ku Beereseba.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Dzina la mwana wake woyamba ndiye Yowele, ndi dzina la wachiwiri ndiye Abiya; ndiwo oweruza a ku Beereseba.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mwana wake wachisamba anali Yowele, wachiŵiri anali Abiya. Iwoŵa ankaweruza ku Beereseba.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mwana wake woyamba anali Yoweli, wachiwiri anali Abiya, ndipo ankaweruza ku Beeriseba.

Onani mutuwo



1 Samueli 8:2
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Abrahamu anabwera kwa anyamata ake, ndipo anauka nayenda pamodzi kumuka ku Beereseba; ndipo anakhala Abrahamu pa Beereseba.


Ndipo Israele anamuka ulendo wake ndi zonse anali nazo, nafika ku Beereseba, napereka nsembe kwa Mulungu wa Isaki atate wake.


Ndipo iye ataona chimenechi, ananyamuka, nathawa kupulumutsa moyo, nafika ku Beereseba wa ku Yuda, nasiya mnyamata wake pamenepo.


ndi Salumu anabala Hilikiya, ndi Hilikiya anabala Azariya,


Ndi ana a Samuele: woyamba Yowele, ndi wachiwiri Abiya.


mwana wa Izihara, mwana wa Kohati, mwana wa Levi, mwana wa Israele.


koma musamafuna Betele, kapena kumalowa mu Giligala; musamapita ku Beereseba; pakuti Giligala adzalowadi m'ndende, ndi Betele adzasanduka chabe.