Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 15:5 - Buku Lopatulika

Ndipo Saulo anafika kumzinda wa Amaleke, nalalira kuchigwa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Saulo anafika kumudzi wa Amaleke, nalalira kuchigwa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndipo Saulo adafika ku mzinda wa Aamaleke, naubisalira m'khwaŵa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Sauli anapita ku mzinda wa Aamaleki nawubisalira mʼkhwawa.

Onani mutuwo



1 Samueli 15:5
4 Mawu Ofanana  

Ndipo anatenga amuna ngati zikwi zisanu, nawaika m'molalira pakati pa Betele ndi Ai, kumadzulo kwa mzinda.


nawalamulira ndi kuti, Taonani, muzikhala olalira kukhonde kwa mzinda; musakhalira kutali ndi mzinda, koma mukhale okonzekeratu nonse;


Ndipo Saulo anamemeza anthu, nawawerenga ku Telaimu, akuyenda pansi zikwi mazana awiri, ndi a kwa Yuda anthu zikwi khumi.


Ndipo Saulo anauza Akeni kuti, Mukani, chokani mutsike kutuluka pakati pa Aamaleke, kuti ndingakuonongeni pamodzi ndi iwo; pakuti inu munachitira ana a Israele onse zabwino, pakufuma iwo ku Ejipito. Chomwecho Akeni anachoka pakati pa Aamaleke.