Yoswa 8:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo anatenga amuna ngati zikwi zisanu, nawaika m'molalira pakati pa Betele ndi Ai, kumadzulo kwa mzinda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo anatenga amuna ngati zikwi zisanu, nawaika m'molalira pakati pa Betele ndi Ai, kumadzulo kwa mudzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Yoswa adapatula anthu zikwi zisanu, naŵabisa cha kuzambwe kwa mzindawo, pakati pa Ai ndi Betele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Yoswa anali atatenga asilikali 5,000 ndi kuwabisa pakati pa Ai ndi Beteli, kumadzulo kwa mzindawo. Onani mutuwo |