Yoswa 8:4 - Buku Lopatulika4 nawalamulira ndi kuti, Taonani, muzikhala olalira kukhonde kwa mzinda; musakhalira kutali ndi mzinda, koma mukhale okonzekeratu nonse; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 nawalamulira ndi kuti, Taonani, muzikhala olalira kukhonde kwa mudzi; musakhalira kutali ndi mudzi, koma mukhale okonzekeratu nonse; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Adaŵapatsa malamulo akuti, “Kabisaleni kumbuyo kwa mzindawo. Musakapite patali ndi mzindawo, koma kakhaleni okonzekera kuuthira nkhondo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 nawapatsa malamulo awa kuti, “Mvetsani bwino; mukabisale kuseri kwa mzindawo. Musakapite patali ndi mzindawo, koma nonsenu mukakhale okonzekera nkhondo. Onani mutuwo |