Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 9:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Muzichita Paska pa nthawi yake yoyikika, madzulo a tsiku la 14 la mwezi uno, potsata malamulo ndi malangizo ake.”

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

3 Tsiku lakhumi ndi chinai la mweziwo, madzulo, muziuchita, pa nyengo yake yoikidwa; muuchite monga mwa malemba ake onse, ndi maweruzo ake onse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Tsiku lakhumi ndi chinai la mweziwo, madzulo, muziuchita, pa nyengo yake yoikidwa; muuchite monga mwa malemba ake onse, ndi maweruzo ake onse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Muzichita Paska tsiku la 14 la mwezi uno, madzulo ake. Muzichita Paskayo potsata malamulo ake ndi malangizo ake onse.”

Onani mutuwo Koperani




Numeri 9:3
10 Mawu Ofanana  

Iwo anapha mwana wankhosa wa Paska pa tsiku la 14 la mwezi wachiwiri. Ansembe ndi Alevi anachita manyazi ndipo anadziyeretsa ndi kubweretsa nsembe zopsereza ku Nyumba ya Yehova.


Mfumu ndi akuluakulu ake pamodzi ndi anthu onse a mu Yerusalemu anagwirizana kuti akondwerere Paska pa mwezi wachiwiri.


Yosiya anachita chikondwerero cha Paska wa Yehova mu Yerusalemu, ndipo mwana wankhosa wa Paska anaphedwa pa tsiku la khumi ndi chinayi la mwezi woyamba.


Yehova anayankhula kwa Mose ndi Aaroni mʼdziko la Igupto kuti,


Chikondwerero cha Paska chiziyamba madzulo a tsiku la 14 la mwezi woyamba.


“Aisraeli azichita Paska pa nthawi yake yoyikika.


Choncho Mose anawuza Aisraeli kuti azichita Paska,


Zikanatero bwenzi Khristu atamva zowawa kambirimbiri chilengedwere cha dziko lapansi. Koma tsopano anaoneka kamodzi kokha chifukwa cha onse pa nthawi yotsiriza kuti achotse tchimo podzipereka yekha nsembe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa