Numeri 7:2 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Kenaka atsogoleri a Aisraeli, akuluakulu a mabanja omwe ankayangʼanira mafuko a anthu omwe anawawerenga aja, anachita chopereka. Onani mutuwoBuku Lopatulika2 akalonga a Israele, akulu a nyumba za makolo ao, anapereka nsembe, ndiwo akalonga a mafuko akuyang'anira owerengedwa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 akalonga a Israele, akulu a nyumba za makolo ao, anapereka nsembe, ndiwo akalonga a mafuko akuyang'anira owerengedwa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Tsiku lomwelo akulu a Aisraele, ndiye kuti atsogoleri a mabanja ndi a mafuko amene ankayang'anira kuŵerenga kuja, Onani mutuwo |