Numeri 10:2 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Sula malipenga awiri a siliva, ndipo uziwagwiritsa ntchito posonkhanitsa anthu pamodzi ndiponso powasamutsa mʼmisasa. Onani mutuwoBuku Lopatulika2 Dzipangire malipenga awiri asiliva; uwasule mapangidwe ake; uchite nao poitana khamu, ndi poyendetsa a m'zigono. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Dzipangire malipenga awiri asiliva; uwasule mapangidwe ake; uchite nao poitana khamu, ndi poyendetsa a m'zigono. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Upange malipenga aŵiri asiliva, uchite kusula. Uziimba malipengawo poitana mpingo, ndi pochoka pa mahema. Onani mutuwo |