Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 1:9 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Eliabu mwana wa Heloni, kuchokera ku fuko la Zebuloni,

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

9 Wa Zebuloni, Eliyabu mwana wa Heloni.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Wa Zebuloni, Eliyabu mwana wa Heloni.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 fuko la Zebuloni, Eliyabu mwana wa Heloni.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 1:9
5 Mawu Ofanana  

Mwa ana a Yosefe: kuchokera ku fuko la Efereimu, Elisama mwana wa Amihudi; kuchokera ku fuko la Manase, Gamalieli mwana wa Pedazuri;


Netanieli mwana wa Zuwara, kuchokera ku fuko la Isakara,


Eliabu mwana wa Heloni ndiye anali mtsogoleri wa fuko la Zebuloni.


Lotsatira lidzakhala fuko la Zebuloni. Mtsogoleri wa gulu la Zebuloni ndi Eliabu mwana wa Heloni.


Pa tsiku lachitatu, Eliabu mwana wa Heloni, mtsogoleri wa Azebuloni, anabweretsa chopereka chake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa