Numeri 1:4 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Munthu mmodzi wochokera ku fuko lililonse yemwe ndi mtsogoleri wa banja lake, ndiye akuthandizeni pa ntchitoyi. Onani mutuwoBuku Lopatulika4 Ndipo pamodzi ndi inu pakhale munthu mmodzi wa mafuko onse; yense mkulu wa nyumba ya kholo lake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo pamodzi ndi inu pakhale munthu mmodzi wa mafuko onse; yense mkulu wa nyumba ya kholo lake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Pa fuko lililonse mutenge munthu mmodzi, mtsogoleri wa banja lake, kuti akuthandizeni pa ntchito yanuyo. Onani mutuwo |