Eksodo 8:1 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Kenaka Yehova anati kwa Mose, “Ukamuwuze Farao kuti, Lolani anthu anga kuti apite, akandipembedze. Onani mutuwoBuku Lopatulika1 Ndipo Yehova anati kwa Mose, Lowa kwa Farao, nunene naye, Atero Yehova, Lola anthu anga amuke, kuti anditumikire. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo Yehova anati kwa Mose, Lowa kwa Farao, nunene naye, Atero Yehova, Lola anthu anga amuke, kuti anditumikire. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pambuyo pake Chauta adalamula Mose kuti, “Pita kwa Farao ukamuuze kuti, Chauta akuti, ‘Uŵalole anthu anga apite akandipembedze. Onani mutuwo |