Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 7:25 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Panapita masiku asanu ndi awiri Yehova atamenya madzi a mu mtsinje wa Nailo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

25 Ndipo anafikira masiku asanu ndi awiri atapanda mtsinje Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Ndipo anafikira masiku asanu ndi awiri atapanda nyanja Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Padapita masiku asanu ndi aŵiri, Chauta ataipitsa mtsinje uja.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 7:25
5 Mawu Ofanana  

Choncho Gadi anapita kwa Davide ndipo anati kwa iye, “Kodi mungakonde kuti mʼdziko mwanu mukhale njala kwa zaka zitatu? Kapena kuti mukhale mukuthawa adani anu kwa miyezi itatu? Kapena kuti mʼdziko muno mukhale mliri kwa masiku atatu? Tsopano, ganizirani bwino ndipo musankhe chomwe mudzamuyankhe amene wandituma.”


Palibe amene anatha kuona mnzake kapena kuchoka pa khomo pake kwa masiku atatu. Koma kumalo kumene kumakhala Aisraeli kunali kowala.


Anthu onse a ku Igupto anayamba kukumba mʼmbali mwa mtsinje wa Nailo kuti apeze madzi akumwa, chifukwa sanathe kumwa madzi a mu mtsinjemo.


Kenaka Yehova anati kwa Mose, “Ukamuwuze Farao kuti, Lolani anthu anga kuti apite, akandipembedze.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa