Eksodo 1:9 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Iyo inati kwa anthu ake, “Taonani, Aisraeli achuluka ndipo ndi amphamvu kwambiri kuposa ife. Onani mutuwoBuku Lopatulika9 Ndipo ananena ndi anthu ake, Taonani, anthu, ndiwo ana a Israele, achuluka, natiposa mphamvu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo ananena ndi anthu ake, Taonani, anthu, ndiwo ana a Israele, achuluka, natiposa mphamvu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Mfumuyo idauza anthu ake kuti, “Aisraeleŵa akuchuluka kwambiri, ndipo ndi amphamvu kupambana ife. Onani mutuwo |