Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 1:2 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Rubeni, Simeoni, Levi, Yuda;

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

2 Rubeni, Simeoni, Levi ndi Yuda;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Rubeni, Simeoni, Levi ndi Yuda;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Rubeni, Simeoni, Levi, Yuda,

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 1:2
5 Mawu Ofanana  

Israeli akanali mʼderali, Rubeni anapita nakagonana ndi Biliha, mdzakazi wa abambo ake. Yakobo uja anazimva zimenezi. Yakobo anali ndi ana aamuna khumi ndi awiri:


Amenewa ndi zidzukulu za Yakobo mwa Biliha amene Labani anapereka kwa mwana wake Rakele. Onse pamodzi analipo asanu ndi awiri.


Awa ndi mayina a ana a Israeli amene anapita ku Igupto pamodzi ndi Yakobo abambo awo, aliyense ndi banja lake:


Isakara, Zebuloni, Benjamini;


Mayina a anthu amene akuthandizeniwo ndi awa: Elizuri mwana wa Sedeuri, kuchokera ku fuko la Rubeni,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa