Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 1:2 - Buku Lopatulika

2 Rubeni, Simeoni, Levi ndi Yuda;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Rubeni, Simeoni, Levi ndi Yuda;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Rubeni, Simeoni, Levi, Yuda,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Rubeni, Simeoni, Levi, Yuda;

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 1:2
5 Mawu Ofanana  

Ndipo panali pamene Israele anakhala m'dzikomo, Rubeni anamuka nagona ndi Biliha, mkazi wamng'ono wa atate wake: ndipo Israele anamva. Ana aamuna a Yakobo anali khumi ndi awiri:


Amenewa ndi ana a Biliha, amene Labani anampatsa Rakele mwana wake wamkazi, amenewo anambalira Yakobo; anthu onse ndiwo asanu ndi awiri.


Ndipo maina a ana a Israele, amene analowa mu Ejipito ndi Yakobo ndi awa, analowa munthu ndi banja lake:


Isakara, Zebuloni, ndi Benjamini;


Ndipo maina a amuna amene aime nanu ndi awa: wa Rubeni, Elizuri mwana wa Sedeuri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa