Danieli 1:16 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Choncho kapitawo anawachotsera chakudya ndi vinyo za ku nyumba yaufumu zija nawapatsa ndiwo zamasamba basi. Onani mutuwoBuku Lopatulika16 Pamenepo kapitaoyo anachotsa chakudya chao ndi vinyo akadamwa, nawapatsa zomera m'nthaka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Pamenepo kapitaoyo anachotsa chakudya chao ndi vinyo akadamwa, nawapatsa zomera m'nthaka. Onani mutuwo |