Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Danieli 1:16 - Buku Lopatulika

16 Pamenepo kapitaoyo anachotsa chakudya chao ndi vinyo akadamwa, nawapatsa zomera m'nthaka.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Pamenepo kapitaoyo anachotsa chakudya chao ndi vinyo akadamwa, nawapatsa zomera m'nthaka.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Choncho kapitawo anawachotsera chakudya ndi vinyo za ku nyumba yaufumu zija nawapatsa ndiwo zamasamba basi.

Onani mutuwo Koperani




Danieli 1:16
2 Mawu Ofanana  

Nati Daniele kwa kapitao, amene mkulu wa adindo adamuikayo ayang'anire Daniele, Hananiya, Misaele, ndi Azariya,


Muyesetu anyamata anu masiku khumi; atipatse zomera m'nthaka tidye, ndi madzi timwe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa