Zekariya 9:6 - Buku Lopatulika6 Ndi mtundu wa anthu osokonezeka udzakhala mu Asidodi, ndipo ndidzaononga kudzikuza kwa Afilisti. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndi mtundu wa anthu osokonezeka udzakhala m'Asidodi, ndipo ndidzaononga kudzikuza kwa Afilisti. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ku Asidodi kudzakhala anthu achimsakaniza. Chauta akuti, “Ndidzathetsa kunyada kwa Filistiya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Mu Asidodi mudzakhala mlendo, ndipo ndidzathetsa kunyada kwa Afilisti. Onani mutuwo |