Zekariya 9:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo ndidzachotsa mwazi wake m'kamwa mwake, ndi zonyansa zake pakati pa mano ake; momwemo iyenso adzakhala wotsalira wa Mulungu wathu, ndipo adzakhala ngati mkulu wa fuko mu Yuda, ndi Ekeroni ngati Myebusi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo ndidzachotsa mwazi wake m'kamwa mwake, ndi zonyansa zake pakati pa mano ake; momwemo iyenso adzakhala wotsalira wa Mulungu wathu, ndipo adzakhala ngati mkulu wa fuko m'Yuda, ndi Ekeroni ngati Myebusi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Anthu ake sadzadyanso nyama yamagazi, kapena nyama yoletsedwa iliyonse. Otsala onse adzakhala anthu anga, adzasanduka ngati fuko la ku Yuda. Nawonso Aekeroni adzakhala ngati Ayebusi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ndidzachotsa nyama ya magazi mʼkamwa mwawo, chakudya choletsedwa mʼmano mwawo. Amene atsala adzakhala anthu a Mulungu wathu, adzasanduka atsogoleri mu Yuda, ndipo Ekroni adzakhala ngati Ayebusi. Onani mutuwo |