Zekariya 9:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo Tiro adzadzimangira polimbikirapo, nadzakundika siliva ngati fumbi, ndi golide woyenga ngati thope la kubwalo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo Tiro adzadzimangira polimbikirapo, nadzakundika siliva ngati fumbi, ndi golide woyenga ngati thope la kubwalo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Tiro adadzimangira linga. Adaunjika siliva ngati dothi, adakundika golide ngati chifwilimbwiti cham'miseu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Ndipo Turo anadzimangira linga; wadziwunjikira siliva ngati fumbi, ndi golide ngati zinyalala za mʼmisewu. Onani mutuwo |