Zekariya 9:2 - Buku Lopatulika2 ndi Hamati yemwe wogundana naye malire; Tiro ndi Sidoni, angakhale ali ndi nzeru zambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 ndi Hamati yemwe wogundana naye malire; Tiro ndi Sidoni, angakhale ali ndi nzeru zambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ndi wa Chautanso mzinda wa Hamati, umene ukuchitana malire ndi maikowo, chimodzimodzinso Tiro ndi Sidoni ngakhale ndi anzeru kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 ndiponso mzinda wa Hamati, umene ukuchita malire ndi dzikoli, komanso pa Turo ndi Sidoni, ngakhale kuti iwo ndi anzeru kwambiri. Onani mutuwo |