Zekariya 8:6 - Buku Lopatulika6 Atero Yehova wa makamu: Chikakhala chodabwitsa pamaso pa otsala a anthu awa masiku awo, kodi chidzakhalanso chodabwitsa pamaso panga? Ati Yehova wa makamu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Atero Yehova wa makamu: Chikakhala chodabwitsa pamaso pa otsala a anthu awa masiku awo, kodi chidzakhalanso chodabwitsa pamaso panga? Ati Yehova wa makamu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 “Ine Chauta Wamphamvuzonse mau anga ndi aŵa: Ngakhale ziwoneke ngati zosatheka kwa anthu a m'fuko limeneli amene adzatsale nthaŵi imeneyo, kodi zimenezi zidzakhalanso zosatheka ndi kwa Ine ndemwe? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Ngati zikuoneka kuti nʼzosatheka kwa anthu otsala pa nthawi ino, kodi zidzakhala zosathekanso kwa Ine?” akutero Yehova Wamphamvuzonse. Onani mutuwo |