Zekariya 8:4 - Buku Lopatulika4 Atero Yehova wa makamu: M'miseu ya Yerusalemu mudzakhalanso amuna ndi akazi okalamba, yense ndi ndodo yake m'dzanja lake chifukwa cha ukalamba wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Atero Yehova wa makamu: M'miseu ya Yerusalemu mudzakhalanso amuna ndi akazi okalamba, yense ndi ndodo yake m'dzanja lake chifukwa cha ukalamba wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 “Ine Chauta Wamphamvuzonse ndikunena kuti, amuna ndi akazi okalamba, oyenda ndi ndodo chifukwa cha ukalamba, adzayendanso m'miseu ya Yerusalemu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Abambo ndi amayi okalamba adzakhalanso mʼmisewu ya mu Yerusalemu, aliyense ali ndi ndodo mʼmanja mwake chifukwa cha kuchuluka kwa masiku ake. Onani mutuwo |