Zekariya 8:16 - Buku Lopatulika16 Izi ndizo muzichite: Nenani choonadi yense ndi mnzake; weruzani zoona ndi chiweruzo cha mtendere m'zipata zanu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Izi ndizo muzichite: Nenani choonadi yense ndi mnzake; weruzani zoona ndi chiweruzo cha mtendere m'zipata zanu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Muzichita izi: muzikambirana zoona, muziweruza moona ndi mwamtendere m'mabwalo a milandu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Zinthu zoti muchite ndi izi: Muziwuzana zoona zokhazokha, muziweruza moona ndi mwachilungamo mʼmabwalo anu; Onani mutuwo |