Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Zekariya 8:15 - Buku Lopatulika

15 momwemonso ndinalingirira masiku ano kuchitira chokoma Yerusalemu ndi nyumba ya Yuda; musaopa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 momwemonso ndinalingirira masiku ano kuchitira chokoma Yerusalemu ndi nyumba ya Yuda; musaopa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Koma masiku ano ndatsimikiza kuti ndimchitira zabwino Yerusalemu ndi banja la Yuda. Choncho musaope.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 “Choncho tsopano ndatsimikiza mtima kuchitiranso zabwino Yerusalemu ndi Yuda. Musachite mantha.

Onani mutuwo Koperani




Zekariya 8:15
10 Mawu Ofanana  

Ndipo padzakhala kuti, monga ndayang'anira iwo kuzula ndi kupasula ndi kugwetsa, ndi kuononga ndi kusautsa; momwemo ndidzayang'anira iwo kumangitsa mudzi ndi kubzala, ati Yehova.


Pakuti atero Yehova: Monga ndatengera anthu awa choipa chonsechi, chomwecho ndidzatengera iwo zabwino zonse ndawalonjeza.


monga momwe ndinapangana nanu muja munatuluka mu Ejipito, ndi Mzimu wanga unakhala pakati pa inu; musamaopa inu.


Ndipo kudzachitika kuti, monga munali chotembereretsa mwa amitundu, inu nyumba ya Yuda, ndi nyumba ya Israele, momwemo ndidzakusungani, ndipo mudzakhala chodalitsa nacho; musaope, alimbike manja anu.


Musaopa, kagulu ka nkhosa inu; chifukwa Atate wanu akonda kukupatsani Ufumu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa