Zekariya 8:15 - Buku Lopatulika15 momwemonso ndinalingirira masiku ano kuchitira chokoma Yerusalemu ndi nyumba ya Yuda; musaopa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 momwemonso ndinalingirira masiku ano kuchitira chokoma Yerusalemu ndi nyumba ya Yuda; musaopa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Koma masiku ano ndatsimikiza kuti ndimchitira zabwino Yerusalemu ndi banja la Yuda. Choncho musaope. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 “Choncho tsopano ndatsimikiza mtima kuchitiranso zabwino Yerusalemu ndi Yuda. Musachite mantha. Onani mutuwo |