Zekariya 8:17 - Buku Lopatulika17 ndipo musalingirira choipa m'mtima mwanu yense pa mnzake; nimusakonde lumbiro lonama; pakuti izi zonse ndidana nazo, ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 ndipo musalingirira choipa m'mtima mwanu yense pa mnzake; nimusakonde lumbiro lonama; pakuti izi zonse ndidana nazo, ati Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Musamachitirane chiwembu, musamakonde kulumbira zonama, pakuti zonsezi ndimadana nazo.” Ndikutero Ine Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 musamachitire mnzanu chiwembu, musamakonde kulumbira zonama. Zonsezi Ine ndimadana nazo,” akutero Yehova. Onani mutuwo |