Zekariya 7:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo pamene mukadya si ndinu, mukamwa si ndinu kodi? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo pamene mukadya si ndinu, mukamwa si ndinu kodi? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Kodi pamene munkadya ndi kumwa, suja munkangodzikondweretsa nokha? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ndipo pamene munkadya ndi kumwa, kodi simunkachita zimenezi podzisangalatsa nokha? Onani mutuwo |