Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Zekariya 6:9 - Buku Lopatulika

9 Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Kenaka Chauta adandipatsa uthenga wakuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Yehova anayankhula nane kuti,

Onani mutuwo Koperani




Zekariya 6:9
3 Mawu Ofanana  

Mwezi wachisanu ndi chitatu, chaka chachiwiri cha Dariusi, mau a Yehova anadza kwa Zekariya mwana wa Berekiya, mwana wa Ido mneneri, ndi kuti,


Ndipo kunachitika chaka chachinai cha mfumu Dariusi, mau a Yehova anadza kwa Zekariya tsiku lachinai la mwezi wachisanu ndi chinai, ndiwo Kisilevi.


Ndipo mau a Yehova wa makamu anadza kwa ine, ndi kuti,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa