Zekariya 6:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo anandiitana, nanena nane, kuti, Taonani, iwo akutuluka kunka kudziko la kumpoto anapumulitsa Mzimu wanga m'dziko la kumpoto. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo anandiitana, nanena nane, kuti, Taonani, iwo akutuluka kunka kudziko la kumpoto anapumulitsa Mzimu wanga m'dziko la kumpoto. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Apo mngeloyo adandiŵuza mokweza mau kuti, “Amene apita ku dziko lakumpotowo atsitsa mzimu wanga kumeneko.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Pamenepo anandiyitana, “Taona, akavalo amene apita ku dziko la kumpoto apumulitsa Mzimu wanga kumeneko.” Onani mutuwo |