Zekariya 6:3 - Buku Lopatulika3 ndi kugaleta wachitatu a kavalo oyera; ndi kugaleta wachinai akavalo olimba amawanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 ndi kugaleta wachitatu a kavalo oyera; ndi kugaleta wachinai akavalo olimba amawanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 lachitatu akavalo oyera, lachinai linkakokedwa ndi akavalo otuŵa a maŵanga ofiirira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 lachitatu ndi akavalo oyera, ndipo lachinayi ndi akavalo otuwa a mawanga ofiirira, onsewa anali akavalo amphamvu kwambiri. Onani mutuwo |